Mkaika CCAP
Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Mkaika CCAP, Health/Beauty, Mkaika ccap box 36 chia nkhotakota, Nkhotakota.
19/04/2026
By Mr malengesa
John 14:24-31 (NIV) - Anyone who does not love me will no | YouVersion Anyone who does not love me will not obey my teaching. These words you hear are not my own; they belong to the Father who sent me. “All this I have spoken while still with you. But the Advocate, the H
📖YOHANE14:27
19/04/2026
Ambuye 'naitana 'ne:
'Dzapumulire kuno,
Tsamira mutu, mwana 'we,
M'chifuwa mwanga muno."
2 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
Wolema, wachisoni;
Anandipulumutsako,
Nakondweretsa ine.
3 Ambuye naitana 'ne:
"Ndipatsa anthu madzi.
Wotopa ndi waludzu 'we,
Dzamwere moyo kuno."
4 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
Ndamwera madzi awa;
Laleka ndithu ludzulo,
Tsopano moyo wadza.
5 Ambuye naitana 'ne:
"La dziko ndine Dzuwa,
Yang'ana Ine, kwacha 'we,
Wachoka mdima uja."
6 Ndayang'anira Mbuyeyo,
Ndapeza Dzuwa langa
Londiyendetsa bwinolo
Pa njira yonse yanga.
19/04/2026
May Manda ndakatulo.taitle (safuna ma existing yaweh)
19/04/2026
Women's choir
19/04/2026
Chibvumbulutso choir
19/04/2026
Sunday school choir
19/04/2026
Grace of God choir
19/04/2026
Betsaida choir
Lero lino m'bale wanga,
Ndilo dzuwa lakukoma;
Talandira Mpulumutsi
M'mene ali kuitana.
2 Lero lino m'bale wanga,
Usazengereza ayi;
Ngati ulandira Yesu
Lero, udzachita mwayi.
3 Lero lino ndi labwino;
Moyo wako uli nawo;
Pena m'mawa umwalira,
Udzatani mlandu wako?
4 Lero lino m'bale wanga,
Lapa mtima, lapa tchimo,
Yesu adzakulandira,
Ukapempha lero lino.
5 Ndiwe mlendo lero lino,
Mvera ndikupempha iwe;
Yesu Mwana wa Mulungu
Akufuna ndithu iwe.
6 Inde, lero lino Yesu
Aitana inu nonse.
Landirani Mpulumutsi,
Musazengereze konse.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Website
Address
Nkhotakota