Symon wazisomo
Advertising your business in this page with affordable price
Nonse amene munatengedwa kuti ndiinu opanda pake Yehova akukumbukileni ,Chisomo chikugwereni kuti awo ozitcha okha amzeru ndi achumawo ukulu wa Mulungu auonere painuππ
Mudzina la Yehova Mulungu wamakamu,afiti onse lero akhale pa tchuti ,asafike pakhomo panu ndipo ndiinu otetedzedwa.ππ
Ngati wakudzutsani ndi moyo lero akupatsaninso zosowa zanu lero.Ameneyo ndiye Yehova Mulungu wamakamu.ππ
Zilibe kanthu kuti zikuoneka ngati nyengo zanu zaipiratu.Koma musafooke ,zikhala bwino ,Yehova alipo.
He is a Lord,he is our savior
Padutsa Zaka khumi dziko lamalawi lilibe mtsogoleri potsatira imfa ya emwe adali mtsogoleri nthawi imeneyo Malemu Bingu Mutharika.Mwina Azasankha mtsogoleri wina mu 2025
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Contact the business
Website
Address
Blantyre
Kabula
BANGWE