Lazaro stezzoh
New comedy videos
19/10/2022
Mumafila uti pa onsewa kwa amene mumaxsata za music
16/06/2022
MWANA NDI BAMBO AKE AGWIDWA NDI CHAMBA
aPolisi ku Ntchisi agwira bambo Zakalia Nyirenda azaka 56 Komanso mwana wawo Lufeyo Zakalia wa zaka 24 chifukwa chopezeka atalima chamba.
M'neneri wa polisi ku Ntchisi Yohane Tasowana watsimikiza za Nkhaniyi ndipo wati awiriwa agwidwa dzulo pa 15 June m'mudzi mwa Kafulu T/A Chilooko m'bomalo.
ATasowana ati patsikuli apolisiwa adatsinidwa khutu ndi 'anyapapi' ena ndipo apolisiwa atathamangila kumaloku adakwanitsa kuzula mitengo 945 ya chamba yomwe ati ayitumiza ku Chitedze Research Station kuti akayipime.
-Naomi Kamiza
16/06/2022
11/06/2022
Moni amalawi ine mwana wanu mwaambuye ndabweranso ndinkhani yoti"""" khalani pompo mumve
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Contact the business
Telephone
Website
Address
Mulanje