ChigweMalawi
People to be remembered in africa
22/12/2024
Iwu ndi msapha omwe mayiko akunja apanga pofuna kukhaulisa malawi kamba kagawo lomwe Malawi yatenga ku nkhondo ya ku Ukraine komanso Gaza, kumbuyo kwa Tanzania kuli mayiko omwe akufuna kukhaulitsa Malawi ๐ฎ
With Manchester City โ I just earned their Top Cityzen badge!
18/09/2024
Genius๐ฅ๐ฅ
Kina phiri titengeni bas๐คธ๐๐ค
11/09/2024
Mabedi wati tilibe tsogolo mu AFCON
Mphunzitsi wa timu ya mpira wamiyendo ya dziko lino, Patrick Mabedi, wabwera poyera kuti pakhala povuta kuti Flames idzipezere malo mu ndime yotsiliza ya mpikitano wa 2025 Africa Cup of Nations (AFCON).
Mabedi walankhula izi atagonja 3-1 ndi timu ya Burkina Faso usiku wathawu ku Bamako, m'dziko la Mali.
"Zikhala zovuta kuti zinthu zitiyendere poyang'anira kuti tiri kumapeto opanda pointi iliyonse. Anzathu zawo zikuyenda ena ali ndi mapointi anayi ena atatu, ife tiribe pointi," watero Mabedi.
Malawi ilibe pointi iliyonse pamasewero awiri omwe yasewera mugulu L lomwe Burkina Faso ndi Senegal akufanana mapointi omwe ndi anayi potengera kuti angosiyana zigoli zomwe achinyitsa komanso zomwe agoletsa.
Burundi ili panambala yachitatu ndi mapointi atatu omwe anatolera atagonjetsa Malawi, pamasewero omwe analipo sabata yatha pa bwalo la Bingu mu nzinda wa Lilongwe.
Wolemba: Richard Tiyesi
Timveni Online ๐ฒ๐ผโ๐ฟโ๐ฟโ๐ฟ
11/09/2024
11/09/2024
๐ค๐ค
Month end ๐คฃ๐ with baby mama
๐คฃ๐คฃ
07/09/2024
I don't want to die alone ๐๐๐
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Website
Address
Thondwe
Zomba