Pido International

Pido International

Share

HUMAN RIGHTS ACTIVIST
FOUNDER OF PIDO INTERNATIONAL ORGANIZATION
HEROS AWARD WINNER OF HUMAN TRAFFICKING IN REPORTING.

06/02/2026

Ya relo: akuti ma office a MEC ku Blantyre atengedwa ndi ozoza. Paichi boma lipeze malo ena okapanga rent.

Kodi mwati, ku lilongwe MEC chavuta ndi chani? Tikudikiranso executive order PARLIAMENT MUST RETURN BACK TO ZOMBA.

06/01/2026

Adad, mkulukutamo kubangula kuti chibwana chanucho muleke. Simungawanyumwise, simungawauze zochita, akukuwoonani, ndipo palibe angawapusise or kuwakhotesa maganizo even wamuchipani chawo. Ndipo achita kulemba kalata dzulo kuti mumvese.

06/01/2026

Chakwera in Jerusalem holy site: Continues with prayer and fasting for ‘better’ Malawi
November 21, 2019 Owen Khamula - Nyasa Times 92 Comments
Malawi Congress Party (MCP) president Lazarus Chakwera has taken time off from attending hectic presidential poll results challenge case to visit Jerusalem as he turned to God by embarking on prayer for “victory over wickedness and for good leaders and truth to reign in Malawi”.

Chakwera in Jerusalem,
In a tweet accompanied by pictures of himself in the Jews and Christian holy land, Chakwera says: “I took a break from court and visited the Church of the Holy Sepelchure in Israel, where I spent some time praying for our beautiful country.”

It is not known how for how long he would be there but party officials say the trip is private.

The Constitutional Court reconvenes next week after a week-long recess for the final leg hearing of the presidential election case.

Anachita kumpitila mulungu pa boma penipeni.

06/01/2026

MEC in Blantyre imapeleka rent, same as they are doing in lilongwe. Ku Blantyre mec ili ndika small office opposite road traffic where by they renting government stores building at wenera clock tower, interms of warehouse, some offices, and any activities of MEC are done there.

When people are backing APM about rentals is senseless and baseless. MEC moved from Blantyre to lilongwe on their own will not any party or political influence, vuto amalawi simufuna kufufuza kuti mudziwe choonadi. You always think, kuti if you are mcp supporter, what ever your leaders are saying it's true and sumungasuse, even if you are DPP supporter, you can oppose the decision. This culture is killing Malawi. APM is a good president yes, but on this executive order he is wrong even mufune musafune. what if APM's oder has happened, later on in 2031,a new president ordered MEC to move to Mangochi? Who will oppose, and what basis will you give? And what if in 2037 a president orders MEC to move to the north, and giving basis saying let our brothers and sisters here to have MEC, MUZASUSA?

tizikhala ndi maganizo awumunthu. On reality MEC supposed to be at center lilongwe despite the political gains or ambitions. In short, that promise was political ambitions but zosapindulisa dziko. Will just waste resources, kulowelera ntchito za MEC, kuchipasa chipani danga.

Say no, to relocation of MEC to Blantyre. Ndizopepela koopsa, ngati bakili kukakamila 3rd term. M***a kutukwana mungathere ku comment section, ine wazimatatu uja, wamanyi nkhonsi uja. But simungasinthe chilungamo because you are in power. Perekani EXECUTIVE ORDER YOLESA KUZIMA KWA MAGESI, NDI FOREX.

06/01/2026

Thyolo timazunzikira Malo ngati sikwathu ,ndipo zomvesa chisoni boma limakhala mbali Ina yotizunzira Malo,ma company ambiri a tea adalanda Malo a wanthu ku Thyolo,kupita Kwa DC sizimaphula kanthu nthawi zonse azungu amawina.

Malo onse mumagulisa kwa anthu obwera, koma mukuzala ukapolo, chifukwa siku lina malo amenewa a zatha and eni dziko a zasowa pogwira. Malo onse mu thyolo, Mulanje anthu adagawana gawana andale, boma lililonse limapezapo phindu popondeleza anthu anu. Mukutenga malo kupeleka kwa obwera omwe kuno sikwawo. TEA amene they claim kuti amalima, akutipinduliranji kuno? We are struggling with forex. Pomwe anthu anakapasidwa malo, mkumalimamo chuma CHATHU chikanasintha, poti food security imathandizira national development.

PIDO International strongly condemns izizi, and malo apite kwa anthu wamba.

06/01/2026

Under Malawi law, a woman who physically beats a man commits an offence in the same manner that any person commits assault, because the law does not distinguish liability based on gender. Where a woman unlawfully slaps, punches, kicks, pushes, or physically attacks a man without causing significant injury, the conduct may amount to Section 253 of the Malawi Penal Code – Common Assault, which is a misdemeanour punishable by imprisonment for up to one (1) year. Where the assault results in physical injuries such as bruises, swelling, cuts, bleeding, or other bodily harm, the offence may fall under Section 254 of the Malawi Penal Code – Assault Occasioning Actual Bodily Harm, which carries a punishment of imprisonment for up to five (5) years. If the attack causes serious or permanent injuries, including fractures or severe wounds, more serious offences relating to grievous harm may arise and attract heavier penalties under the Penal Code. In determining the offence and punishment, the court considers the nature of the violence, the extent of injuries sustained, medical evidence, witness testimony, and the surrounding circumstances of the incident. “And this woman must be arrested without a warrant…. A Man Has Been Abused Where are you Human Rights Activists and Defenders Where are you !!!!

Pido International.

05/31/2026

KODI MWATI ZOTI " MEC" ISAMUKILE KU BLANTYRE ZILI NDIPHINDU LANJI?

05/31/2026

Pido International, ndi bungwe lomwe limamenyera ufulu both males and females. Ndipo khumbo lake ndi kuonesesa kuti chilungamo chikusatidwa. Kusatila video yomwe ikuyenda pamasamba amchezo, khuda ikena muyawa, wamenyedwa, kunyazisidwa, kutukwanidwa(insulting) zomwe ndi milandu pa malamulo a dziko lino. Pachifukwa ichi, pido International we calling police, to arrest the lady, and mabungwe anzathu kuwoonesesa kuti chilungamo chioneke and lamulo lagwira mchito pa a chemwaliwa.

Zisakhale zophweka chifukwa wachita izi ndi mkazi kwa mwamuna, zoterezi zikuchitisa kuti azibambo azizipha chifukwa or akatule nkhawa zawo anthu sachitapo kanthu koma akhale kaye mkazi. Imagine khuda, anakabweza ndi khofi kwa mkazi uja, social media lero nkhani ili yokakamiza khuda kuti amangidwe, pomenya mkazi. Lero mkazi wamenya mwamuna, ndi chifukwa pido international yadzuka monga inachitira ndi Jomo atamenya mzimayi.

Yes analakwirana anthuwo, koma sizimayenera kuti azisove mwantundu oterewu, sitikungozuzula kokha, komaso kuyitanila lamulo kuti ligwire ntchito, ndipo sitipuma mpaka mkazi uyuyu atamangidwa, milandu yomwe wapalamula apapa ndiyayikulu ku constitution ya dziko. Tilibe mbali pakumenyera ufulu, sitizayikira munthu kumbuyo, koma kuima pa chilungamo. Khuda ikena muyawa deserves chilungamo, if tili anthu osata malamulo.

Looking forward to see actions from Malawi police.

05/31/2026

Mwamukumbukira Mathew’s?
Nnapasidwa nkhani ya Mathew’s ndi Hope Mwanavava kuti aludwara diabetes koma akusowa Thandizo ndi makhwara i told him let me post kuti tipeze helper wake chifukwa panthawi yo ku Pido international organization too Ali ndi anthu ena sono Poona kuti Mathew’s need help as soon as possible nnabweletsa pano ena anagulako makhwara ndipo ena anasonkha 50 thousand kwacha ndipo ambiri munapanga tag Tusa Yana ndipo anabweta Nkumutenga Kuti amuthandize Pokhara naye, lero ndangoona Hope Mwanavava wapanga post kuti rest in peace Mathew’s zosakhara bwino. May Mathew’ss soul rest in peace, may God strengthen the family,
Thank you so much Tusa for your kind hearted, thanks everyone that contributed and prayed for him May God Richly bless you. And of course God bless me for being a bridge may he remember my name. Amen 🙏

Rest in peace Mathew’s .

05/31/2026

Koma mwati mpaka ku Rwanda kophuzisana njinga? Kuti ifeo tatani? Moti ngozi zosenzi nkhani ndikusatha njinga or kusasata malamulo? Kapena ku Rwanda akukawaphuzinsa kusata malamulo osati njinga? Munthu akunyamula anthu 4 njinga imodzi, mu high way, nkhani ndi kusatha or kusamvera malamulo?

Road traffic mutumizeso ama minibus, amasiyenta, asozi chifukwa zikuwooneka kuti ndalama (forex) tili nazo nzochuluka kwambiri, zatipepetula.

Want your business to be the top-listed Beauty Salon in Manchester?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Category

Website

Address


Manchester, NH
03103