Pido International
HUMAN RIGHTS ACTIVIST
FOUNDER OF PIDO INTERNATIONAL ORGANIZATION
HEROS AWARD WINNER OF HUMAN TRAFFICKING IN REPORTING.
Pan Africa mining limited kudzera mwa wankulu wake Suresh leddy, yawuza amalawi lero masanawa kuti company yawo inakumba myala 2.5 tonnes kutipita nawo kwawo kuti akayeze ngatidi malowa ku Dowa pali Granite. Ndipo akulu akulu a nkhosolo ya Dowa ndi aku mining anamwemwetera kuti mweeeeee.
Koma kodi zimafunika kuchuluka kotani kuti ayeze myalayi? Is it 2kg 10 kg, half tonne, or 50 tonnes Kapena mgodi onse?
Nanga, anayeza ndi ndani kuti pamalowa pali granite? Ndipo why pan Africa ikufuna kukayezesa myalayi kuti isimikize? Ndiye kuti onama ndi yemwe anatiuza yo or awawa Kapena ministry of mining ikutinamiza?
Malawi bwenzi atalemera kale ndi myala. Koma mawu oti kuyeza ndiwo akutisaukisa. Kayerekera anatha uranium yense ndikuyeza mpaka pano palibe chomwe tinapindulapo. Ulendo uno tikupusisidwabwe. Ine kuwoona ngati alipo omwe amapindula chifukwa ku ministry ko sangalephere kuziwa kuti uwu ndi usiru omatenga myala in the name of kukayeza.
Tipempha mbuye, Mutidikire mwina Asintha, Dzikoli musawotche moto.
Nkhani ya mayi Brenda Driemo ilipati?
Zimvereni nokha umboni. Chitukuko chili mdera lake, iye okhala mtsogoleri akukabaso zipangizo zachitukuko. Palibwino mwati? Ndiye China muchimva chikuti ndi ndale eeee amamumanga kuti athane naye aaaaaaaaa. Koma apapa pali any influence from DPP to arrest the MP? Kupusa.
Tipempha mbuye, Mutidikire mwina Asintha, Dzikoli musawotche moto.
Pido International # # #
06/25/2026
Ndiye kuli awaa. Zogunata zeni zeni. Ati report la hotel lili ready ndipo latheka. Koma are you srs as a competent chair, a patriotic citizen and MZIKA yokonda dziko lake? Kodi inu, umunthu mwasiya kuti?
Report lipsa /litheka bwanji without Mrs ZAMBA, without Yusuf mwina wake wa hotel, without Magalasi. Awawa ndiye ma key prayers ndipo without awawa report limenelo lili chabe ndipo siliyankha chaphindu kwa amalawi. Moti mukufuna anthu azabwerezenso inquiry kena, ngati ya ndege? Anatilozayo eeeeeee ayi. Koma agaru awawa
Tipempha mbuye, Mutidikire mwina Asintha, Dzikoli musawotche moto.
Pido International # # #
06/25/2026
Usakhale ndi phuma ngati ine kutuluka mu DPP munthawi yanga. You're the Ansah to hopeless Malawians. Ukhale konko wamva. Adatero Amphavu mwaife kuuza madam madando form 62
06/24/2026
Mukudikila chiphe kaye anthu then muzatinyasepo ndi ma inquiry et. Adachipanga ku Scotland mu 1949 ndipo chidayamba kuyenda pa lake Malawi mu 1951. Adachipasa life span ya 70 years. Mpaka lero chili pa madzi kunyamula miyoyo ya anthu.
Chikapha anthu ndiye ma inquiry chikhalilecho vuto mukungoliyang'inila. Ndife fuko loyenera kukakhala ku meseum, chifukwa ndife fuko lopasisa chidwi mzochitika zathu.
06/24/2026
A Dad koma mwakhalisa chete and sizikukoma. Kodi zikuchitikazi koma mwati APM amaziwoona? News paper mwati munthuyi amamupasa? Nanga akawoona zomwe zikuchika amati chani? Ndipo ndi ndani amawanamiza apule and reason yake nivichi?
Usawi uwu wakhalisa kwazaka zaka ndipo ngati dziko sitikupindula koma omwewo mweo ndiye akulemelera daily. A kugula malo 800 million, ndiye nyumba yozamangidwayo izakhala yama billion angati? Ndipo apeza kuti? Liti? Amatani?
Apule, pena usiru uwuuu mukuwukolezera nokha, powombera mmanja ng'ona zamam'bango. Nduna zomwe zili pampikisano wakuba ndizo mumazisekelera ndikuzisasatisa muli zimatha nchito. Ayi aaaaaaaaaa arefu nthawi. Mbava izoooooo under proven leadership πππππππ.
Comment sections is open, nditukwaneni mungathere agaru okuba inu. I'm here to read every comment. But DPP is stealing from us, poor people, sad nation. Zoti chuma chizuka aaaaaaaaaa tabalotani
06/24/2026
DPP indeed it's a system
DPP changes the plans on how to steal from poor Malawians. They are using now rotten system of government to kill Malawi. They are hypocritical, paguru akuti they are fixing the economy but the reality is, they messing up the economy.
Since they took the proven leadership government, how many BILLIONS WE LOST?
- we have to pay muli brothers billions.
- we have to pay finance bank billions.
- we have robbed 128 billion from hotel saga, and the big players are the DPP gurus.
- we have to pay salima sugar alot of billions
- we have to pay again to escom for spare parts which we paid it already and they chose to mess up.
List is endless. Zonsezi it's all about system. And amazitamilira kuti ndi system ndipo akususa ndani that is a system?
Ulendo uno ndalama zizitulukira mumakhoti, ndipo aliyense wachipani Cha DPP who convicted with mcp government, has a possibility of being a route of taking billions from poor Malawians. Ndipo milandu yambiri ithera " pay this one"
Pido
06/24/2026
Malawi Parliament is a scarm.
What was the purpose of Public Accounts Committee (PAC) in Amaryllis Scandal.
You canβt Cheat 22 Million people.
DPP was grossly involved in the theft of pension money. Nobody from DPP has been touched. They are busy telling us that they are working to turn around the economy. What a silly joke.
Akuti poverty levels are coming down. Inflation is easing. Says a country with no forex.
Hon Baba Steven K Malondera how far or near are you with the Report?
Now that the Court has unfrozen the Amarylis Bank Accounts what other recourse is there to salvage the situation?
Kuli ziiii, nanga about Colin Zamba zilipati? Who hold this house accountable koma?
Pido International report # # #
06/24/2026
Apolice amanga phungu wanyumba yamalamulo wa ku mzimba south mkamba koba quarry mu 2021. A jere, posachedwapa anali nawo mgulu lotenga injunction yolesa MEC kusamukira ku Blantyre.
Kodi zikafika apa mumatani? Ngati phungu akupezeka akuba or kugula zakuba, angapange lamulo lothandiza MZIKA zake ku Parliament? Aphungu ngati awa ngochuluka bwanji?
Posakhalisanso phungu wina waku nkhotakota, sylvester ayuba James anapezeka otabela client wake ndalama. Aphungu ngati amenewa Malawi angamutengere kuti?
Pido International report.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Website
Address
Manchester, NH
03103